Skip to content

Rosemary Tembo

Organization BSM

Pays Malawi

Région Afrique centrale

Secteur Lifelong Learning

Poste / titre du poste Assistant Literacy Coordinator

map

My experience in adult learning and education

Akulu akulu nthawi zambiri amaphunzira ndi cholinga, amakhala ndi Chidwi kuti chomwe akufuna kuphunzira achidziwe, amafuna kulemekezedwa komanso amafuna muwathandize kuchoka ku zomwe amadziwa kufika ku zinthu zomwe sakudziwa. Munthu wamkulu safuna kukalipidwa, amasatira zinthu pena mwachangu ndipo ena mochedwa koma onsewa amafunikira kuti muyende ndi kuwathandizira limodzi malingana ndi kuthekera kwao. Amenewa amasiyana ndi ana choncho mphunzitsi asamawatenge ngati ndi ana. Sukulu simatha akulu akulu amaphunzira pena Poona, kulemba komanso kuchita nawo. Kuphunzira kwao kumafunikiranso masangulutso kuti socially azikhala olumbikitsika komanso mentally alert.